Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 2:8 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

8 Chiwerengero cha gulu lake lankhondo ndi 57,400.

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

8 Ndi khamu lake, ndi owerengedwa ake, ndiwo zikwi makumi asanu mphambu zisanu ndi ziwiri kudza mazana anai.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

8 Ndi khamu lake, ndi owerengedwa ake, ndiwo zikwi makumi asanu mphambu zisanu ndi ziwiri kudza mazana anai.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

8 ndipo ankhondo ake ngokwanira 57,400.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 2:8
4 Mawu Ofanana  

Chiwerengero cha anthu ochokera mʼfuko la Zebuloni chinali 57,400.


Lotsatira lidzakhala fuko la Zebuloni. Mtsogoleri wa gulu la Zebuloni ndi Eliabu mwana wa Heloni.


Anthu onse aamuna mʼmisasa ya Yuda, chiwerengero chawo ndi 186,400 monga mwa magulu awo. Iwowo ndiwo aziyamba kusamuka.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa