Numeri 2:14 - Buku Lopatulika14 Ndi fuko la Gadi; kalonga wa ana a Gadi ndiye Eliyasafu mwana wa Reuwele. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Ndi fuko la Gadi; kalonga wa ana a Gadi ndiye Eliyasafu mwana wa Reuwele. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Tsono pabwere fuko la Gadi, limene mtsogoleri wake ndi Eliyasafu, mwana wa Deuwele, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Lotsatira lidzakhala fuko la Gadi. Mtsogoleri wa gulu la Gadi ndi Eliyasafu mwana wa Deuweli. Onani mutuwo |