Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 2:14 - Buku Lopatulika

14 Ndi fuko la Gadi; kalonga wa ana a Gadi ndiye Eliyasafu mwana wa Reuwele.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

14 Ndi fuko la Gadi; kalonga wa ana a Gadi ndiye Eliyasafu mwana wa Reuwele.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

14 Tsono pabwere fuko la Gadi, limene mtsogoleri wake ndi Eliyasafu, mwana wa Deuwele,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

14 Lotsatira lidzakhala fuko la Gadi. Mtsogoleri wa gulu la Gadi ndi Eliyasafu mwana wa Deuweli.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 2:14
6 Mawu Ofanana  

Wa Gadi, Eliyasafu mwana wa Deuwele.


Ndi pa gulu la fuko la ana a Gadi anayang'anira Eliyasafu mwana wa Deuwele.


Ndi khamu lake ndi owerengedwa ake, ndiwo zikwi makumi asanu mphambu zisanu ndi zinai kudza mazana atatu.


Ndi khamu lake, ndi owerengedwa ake, ndiwo zikwi makumi anai mphambu zisanu kudza mazana asanu ndi limodzi mphambu makumi asanu.


Tsiku lachisanu ndi chimodzi kalonga wa ana a Gadi, Eliyasafu mwana wa Deuwele:


ndi nsembe yoyamika, ng'ombe ziwiri, nkhosa zamphongo zisanu, atonde asanu, anaankhosa asanu a chaka chimodzi; ndicho chopereka cha Eliyasafu mwana wa Deuwele.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa