Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 2:13 - Buku Lopatulika

13 Ndi khamu lake ndi owerengedwa ake, ndiwo zikwi makumi asanu mphambu zisanu ndi zinai kudza mazana atatu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

13 Ndi khamu lake ndi owerengedwa ake, ndiwo zikwi makumi asanu mphambu zisanu ndi zinai kudza mazana atatu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

13 ndipo ankhondo ake ngokwanira 59,300.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

13 Chiwerengero cha gulu lake lankhondo ndi 59,300.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 2:13
4 Mawu Ofanana  

owerengedwa ao a fuko la Simeoni, ndiwo zikwi makumi asanu mphambu zisanu ndi zinai kudza mazana atatu.


Ndipo iwo akumanga mahema ao poyandikizana naye ndiwo a fuko la Simeoni; ndi kalonga wa ana a Simeoni ndiye Selumiele mwana wa Zurishadai.


Ndi fuko la Gadi; kalonga wa ana a Gadi ndiye Eliyasafu mwana wa Reuwele.


Iwo ndiwo mabanja a Asimeoni, zikwi makumi awiri mphambu ziwiri kudza mazana ziwiri.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa