Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Numeri 2:13 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

13 Chiwerengero cha gulu lake lankhondo ndi 59,300.

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

13 Ndi khamu lake ndi owerengedwa ake, ndiwo zikwi makumi asanu mphambu zisanu ndi zinai kudza mazana atatu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

13 Ndi khamu lake ndi owerengedwa ake, ndiwo zikwi makumi asanu mphambu zisanu ndi zinai kudza mazana atatu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

13 ndipo ankhondo ake ngokwanira 59,300.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 2:13
4 Mawu Ofanana  

Chiwerengero cha anthu ochokera mʼfuko la Simeoni chinali 59,300.


Fuko la Simeoni lidzamanga pafupi ndi Rubeni. Mtsogoleri wa gulu la Simeoni ndi Selumieli mwana wa Zurisadai.


Lotsatira lidzakhala fuko la Gadi. Mtsogoleri wa gulu la Gadi ndi Eliyasafu mwana wa Deuweli.


Awa anali mafuko a Simeoni. Iwowa analipo amuna 22,200.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa