Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 2:15 - Buku Lopatulika

15 Ndi khamu lake, ndi owerengedwa ake, ndiwo zikwi makumi anai mphambu zisanu kudza mazana asanu ndi limodzi mphambu makumi asanu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

15 Ndi khamu lake, ndi owerengedwa ake, ndiwo zikwi makumi anai mphambu zisanu kudza mazana asanu ndi limodzi mphambu makumi asanu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

15 ndipo ankhondo ake ngokwanira 45,650.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

15 Chiwerengero cha gulu lake lankhondo ndi 45,650.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 2:15
4 Mawu Ofanana  

owerengedwa ao a fuko la Gadi, ndiwo zikwi makumi anai mphambu zisanu kudza mazana asanu ndi limodzi mphambu makumi asanu.


Ndi fuko la Gadi; kalonga wa ana a Gadi ndiye Eliyasafu mwana wa Reuwele.


Owerengedwa onse a chigono cha Rubeni ndiwo zikwi makumi khumi mphambu makumi asanu ndi chimodzi kudza mazana anai mphambu makumi asanu, monga mwa makamu ao. Ndiwo azitsatana nao otsogolerawo.


Iwo ndiwo mabanja a ana a Gadi, monga mwa owerengedwa ao, zikwi makumi anai ndi mazana asanu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa