Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Numeri 2:14 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

14 Lotsatira lidzakhala fuko la Gadi. Mtsogoleri wa gulu la Gadi ndi Eliyasafu mwana wa Deuweli.

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

14 Ndi fuko la Gadi; kalonga wa ana a Gadi ndiye Eliyasafu mwana wa Reuwele.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

14 Ndi fuko la Gadi; kalonga wa ana a Gadi ndiye Eliyasafu mwana wa Reuwele.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

14 Tsono pabwere fuko la Gadi, limene mtsogoleri wake ndi Eliyasafu, mwana wa Deuwele,

Onani mutuwo Koperani




Numeri 2:14
6 Mawu Ofanana  

Eliyasafu mwana wa Deuweli, kuchokera ku fuko la Gadi,


ndipo Eliyasafu mwana wa Deuweli ndiye ankatsogolera fuko la Gadi.


Chiwerengero cha gulu lake lankhondo ndi 59,300.


Chiwerengero cha gulu lake lankhondo ndi 45,650.


Pa tsiku lachisanu ndi chimodzi, Eliyasafu mwana wa Deuweli, mtsogoleri wa fuko la Gadi, anabweretsa chopereka chake.


ngʼombe zazimuna ziwiri, nkhosa zazimuna zisanu, mbuzi zazimuna zisanu ndi ana ankhosa aamuna asanu a chaka chimodzi, nsembe yachiyanjano. Ichi chinali chopereka cha Eliyasafu mwana wa Deuweli.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa