Numeri 17:7 - Buku Lopatulika7 Ndipo Mose anaika ndodozo pamaso pa Yehova m'chihema cha mboni. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Ndipo Mose anaika ndodozo pamaso pa Yehova m'chihema cha mboni. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Mose adakaziika ndodozo pamaso pa Chauta m'chihema chaumboni. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Mose anayika ndodozo pamaso pa Yehova mu tenti ya msonkhano. Onani mutuwo |