Numeri 11:6 - Buku Lopatulika6 koma tsopano moyo wathu waphwa; tilibe kanthu pamaso pathu koma mana awa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 koma tsopano moyo wathu waphwa; tilibe kanthu pamaso pathu koma mana awa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Koma tsopano mphamvu zathu zatha, ndipo sitikuwona kanthu kena kakudya koma mana basi.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Koma tsopano chilakolako chathu chatha. Sitikuona kanthu kena kakudya koma mana basi!” Onani mutuwo |