Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 10:7 - Buku Lopatulika

7 Pomemeza msonkhano mulize, wosati chokweza ai.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

7 Pomemeza msonkhano mulize, wosati chokweza ai.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

7 Pamene mpingo wonse uyenera kusonkhana pamodzi, mulize lipenga, koma musalize lipenga lochenjeza.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

7 Pofuna kusonkhanitsa anthu, muziliza malipenga, koma mosiyana ndi mmene malipenga ochenjeza amalizidwira.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 10:7
3 Mawu Ofanana  

Muombe lipenga mu Ziyoni, nimufuulitse m'phiri langa lopatulika; onse okhala m'dziko anjenjemere; pakuti tsiku la Yehova lilinkudza, pakuti liyandikira;


Ana aamuna a Aroni, ansembe, ndiwo aziliza malipenga; ndipo akhale kwa inu lemba losatha ku mibadwo yanu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa