Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 10:8 - Buku Lopatulika

8 Ana aamuna a Aroni, ansembe, ndiwo aziliza malipenga; ndipo akhale kwa inu lemba losatha ku mibadwo yanu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

8 Ana amuna a Aroni, ansembe, ndiwo aziliza malipenga; ndipo akhale kwa inu lemba losatha ku mibadwo yanu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

8 Ana a Aroni, ansembe aja, ndiwo aziliza malipenga. Ntchito ya malipengayi ndi lamulo lamuyaya pa mibadwo yanu yonse.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

8 “Ana a Aaroni, ansembe aja, ndiwo aziliza malipengawo. Zimenezi zikhale zokhazikika kwa inu ndi ku mibado yanu yonse.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 10:8
5 Mawu Ofanana  

Ndi Sebaniya, ndi Yosafati, ndi Netanele, ndi Amasai, ndi Zekariya, ndi Benaya, ndi Eliyezere, ansembe, analiza malipenga ku likasa la Mulungu; ndi Obededomu ndi Yehiya anali odikira a likasa.


ndi Benaya ndi Yahaziele ansembe ndi malipenga kosalekeza, ku likasa la chipangano la Mulungu.


Ndipo Mose anawatuma a fuko limodzi chikwi chimodzi, kunkhondo, iwowa ndi Finehasi mwana wa Eleazara wansembe, kunkhondo, ndi zipangizo zopatulika, ndi malipenga oliza m'dzanja lake.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa