Numeri 10:7 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Pofuna kusonkhanitsa anthu, muziliza malipenga, koma mosiyana ndi mmene malipenga ochenjeza amalizidwira. Onani mutuwoBuku Lopatulika7 Pomemeza msonkhano mulize, wosati chokweza ai. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Pomemeza msonkhano mulize, wosati chokweza ai. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Pamene mpingo wonse uyenera kusonkhana pamodzi, mulize lipenga, koma musalize lipenga lochenjeza. Onani mutuwo |