Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 10:18 - Buku Lopatulika

18 Ndi a mbendera ya chigono cha Rubeni, anayenda monga mwa magulu ao; ndipo pa gulu lake anayang'anira Elizuri mwana wa Sedeuri.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

18 Ndi a mbendera ya chigono cha Rubeni, anayenda monga mwa magulu ao; ndipo pa gulu lake anayang'anira Elizuri mwana wa Sedeuri.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

18 Pambuyo pake otsata mbendera ya zithando za fuko la Rubeni adanyamuka m'magulumagulu, ndipo mtsogoleri wa gulu lao anali Elizuri mwana wa Sedeuri.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

18 Kenaka magulu a msasa wa fuko la Rubeni ananyamuka potsatira mbendera yawo. Mtsogoleri wawo anali Elizuri mwana wa Sedeuri.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 10:18
6 Mawu Ofanana  

Ndipo maina a amuna amene aime nanu ndi awa: wa Rubeni, Elizuri mwana wa Sedeuri.


Ndi pa gulu la fuko la ana a Simeoni anayang'anira Selumiele mwana wa Zurishadai.


Mukalizanso chokweza, a m'zigono za kumwera ayende; alize chokweza pakumuka.


ndi nsembe yoyamika, ng'ombe ziwiri, nkhosa zamphongo zisanu, atonde asanu, anaankhosa asanu a chaka chimodzi; ndicho chopereka cha Elizuri mwana wa Sedeuri.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa