Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 10:19 - Buku Lopatulika

19 Ndi pa gulu la fuko la ana a Simeoni anayang'anira Selumiele mwana wa Zurishadai.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

19 Ndi pa gulu la fuko la ana a Simeoni anayang'anira Selumiele mwana wa Zurishadai.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

19 Mtsogoleri wa gulu la Asimeoni anali Selumiele mwana wa Zurishadai.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

19 Mtsogoleri wa fuko la Simeoni anali Selumieli mwana wa Zurisadai,

Onani mutuwo Koperani




Numeri 10:19
4 Mawu Ofanana  

Wa Simeoni, Selumiele mwana wa Zurishadai.


Ndi a mbendera ya chigono cha Rubeni, anayenda monga mwa magulu ao; ndipo pa gulu lake anayang'anira Elizuri mwana wa Sedeuri.


Ndi pa gulu la fuko la ana a Gadi anayang'anira Eliyasafu mwana wa Deuwele.


Tsiku lachisanu kalonga wa ana a Simeoni, ndiye Selumiele, mwana wa Zurishadai:


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa