Numeri 1:53 - Buku Lopatulika53 Koma Alevi amange mahema ao pozungulira pa chihema cha mboni, kuti mkwiyo ungagwere khamu la ana a Israele; ndipo Alevi azidikira chihema cha mboni. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201453 Koma Alevi amange mahema ao pozungulira pa Kachisi wa mboni, kuti mkwiyo ungagwere khamu la ana a Israele; ndipo Alevi azidikira Kachisi wa mboni. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa53 Koma Alevi amange mahema ao pozungulira chihema chaumboni, kuti Mulungu asakwiyire mpingo wa Aisraele. Alevi ndiwo amene aziyang'anira chihema chaumbonicho.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero53 Alevi nawonso, azimanga matenti awo mozungulira tenti yopatulika kuti chilango chisagwere Aisraeli onse. Ndipo Alevi aziyangʼanira ndi kusamalira tenti yopatulikayo.” Onani mutuwo |