Mlaliki 6:9 - Buku Lopatulika9 Kupenya kwa maso kuposa kukhumba kwa mtima; ichinso ndi chabe ndi kungosautsa mtima. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Kupenya kwa maso kuposa kukhumba kwa mtima; ichinso ndi chabe ndi kungosautsa mtima. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Kuli bwino kumangopenya zinthu ndi maso kupambana kumazilakalaka chamumtima. Zimenezinso nzopanda phindu, ndipo kuyesa kuzimvetsa nkungodzivuta chabe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Kuli bwino kumangoona zinthu ndi maso kusiyana ndi kumangozilakalaka mu mtima. Izinso ndi zopandapake, nʼkungodzivuta chabe. Onani mutuwo |