Mlaliki 6:10 - Buku Lopatulika10 Chomwe chinalipo chatchedwa dzina lake kale, chidziwika kuti ndiye munthu; sangathe kulimbana ndi womposa mphamvu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Chomwe chinalipo chatchedwa dzina lake kale, chidziwika kuti ndiye munthu; sakhoza kulimbana ndi womposa mphamvu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Chilichonse chimene chilipo adachitchula kale dzina. Za m'mene munthu aliri nzodziŵika, nchomveka kuti sangathe kutsutsana ndi amene ali wamphamvu kupambana iyeyo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Chilichonse chimene chilipo anachitchula kale dzina, za mmene munthu alili nʼzodziwika; sangathe kutsutsana ndi munthu amene ali wamphamvu kupambana iyeyo. Onani mutuwo |