Mlaliki 6:8 - Buku Lopatulika8 Pakuti wanzeru ali ndi chiyani choposa chitsiru? Waumphawi wodziwa kuyenda pamaso pa amoyo ali ndi chiyani? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Pakuti wanzeru ali ndi chiyani choposa chitsiru? Waumphawi wodziwa kuyenda pamaso pa amoyo ali ndi chiyani? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Nanga munthu wanzeru ali ndi chiyani chimene amapambana nacho chitsiru? Kodi mmphaŵi amene amangodziŵa kukhala bwino pamaso pa anzake, ndiye kuti wapindulapo chiyani? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Kodi munthu wanzeru amaposa motani chitsiru? Kodi munthu wosauka amapindula chiyani podziwa kukhala bwino pamaso pa anthu ena? Onani mutuwo |