Mlaliki 6:7 - Buku Lopatulika7 Ntchito zake zonse munthu angogwirira m'kamwa mwake, koma mtima wake sukhuta. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Ntchito zake zonse munthu angogwirira m'kamwa mwake, koma mtima wake sukhuta. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Munthu amagwira ntchito zolemetsa kuti apeze chakudya, komabe satha kukhutira kotheratu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Ntchito yonse ya munthu imathera pakamwa pake, komatu iye sakhutitsidwa ndi pangʼono pomwe. Onani mutuwo |