Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mlaliki 6:4 - Buku Lopatulika

4 pakuti ikudza mwachabe, nichoka mumdima, mdima nukwirira dzina lake.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

4 pakuti ikudza mwachabe, nichoka mumdima, mdima nukwirira dzina lake.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

4 Mtayo umangopita pachabe nkuloŵa mu mdima, ndipo umakaiŵalika mumdimamo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

4 Mtayo umangopita pachabe ndipo umapita mu mdima, ndipo mu mdimamo dzina lake limayiwalika.

Onani mutuwo Koperani




Mlaliki 6:4
3 Mawu Ofanana  

Zidzukulu zake zidulidwe; dzina lao lifafanizidwe mu mbadwo ukudza.


Chinkana munthu akabala ana makumi khumi, nakhala ndi moyo zaka zambiri, masiku a zaka zake ndi kuchuluka, koma mtima wake osakhuta zabwino, ndiponso alibe maliro; nditi, Nsenye iposa ameneyo;


Ngakhale dzuwa siliona ngakhale kulidziwa, imeneyi ipambana winayo kupuma;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa