Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mlaliki 6:5 - Buku Lopatulika

5 Ngakhale dzuwa siliona ngakhale kulidziwa, imeneyi ipambana winayo kupuma;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

5 Ngakhale dzuwa siliona ngakhale kulidziwa, imeneyi ipambana winayo kupuma;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

5 Ngakhale mtayowo sudaone dzuŵa kapena kudziŵa kanthu kalikonse, komabe umapumula kupambana munthu wa moyo wautali uja,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

5 Ngakhale kuti mtayowo sunaone dzuwa kapena kudziwa kanthu kalikonse, koma umapumula kuposa munthu uja,

Onani mutuwo Koperani




Mlaliki 6:5
8 Mawu Ofanana  

Munthu wobadwa ndi mkazi ngwa masiku owerengeka, nakhuta mavuto.


Apite ngati nkhono yosungunuka; asaone dzuwa monga mtayo.


Indetu kuunika nkokoma, maso napeza bwino m'kuona dzuwa.


inde yemwe sanabadwe konse aposa onse awiriwo popeza sanaone ntchito yoipa yochitidwa kunja kuno.


pakuti ikudza mwachabe, nichoka mumdima, mdima nukwirira dzina lake.


akakhala ndi moyo zaka zikwi ziwiri, koma osakondwera; kodi onse sapita kumalo amodzi?


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa