Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mlaliki 6:1 - Buku Lopatulika

1 Pali choipa ndachiona kunja kuno chifalikira mwa anthu,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

1 Pali choipa ndachiona kunja kuno chifalikira mwa anthu,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

1 Choipa china chimene ndachiwona pansi pano, chimene chimaŵaŵa anthu zedi, ndi ichi:

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

1 Ine ndinaona choyipa china pansi pano, ndipo chimasautsa anthu kwambiri:

Onani mutuwo Koperani




Mlaliki 6:1
2 Mawu Ofanana  

Pali choipa chovuta ndachiona kunja kuno, ndicho, chuma chilikupweteka eni ake pochikundika;


munthu amene Mulungu wamlemeretsa nampatsa chuma ndi ulemu, mtima wake susowa kanthu kena ka zonse azifuna, koma Mulungu osampatsa mphamvu ya kudyapo, koma mlendo adyazo; ichi ndi chabe ndi nthenda yoipa.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa