Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Mlaliki 5:20 - Buku Lopatulika

20 Pakuti sadzakumbukira masiku a moyo wake kwambiri; chifukwa Mulungu amvomereza m'chimwemwe cha mtima wake.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

20 Pakuti sadzakumbukira masiku a moyo wake kwambiri; chifukwa Mulungu amvomereza m'chimwemwe cha mtima wake.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

20 Munthu wotereyu sadzaganizako kwenikweni za kuchepa kwa masiku a moyo wake, chifukwa chakuti Mulungu wamdzaza ndi chimwemwe mu mtima.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

20 Munthu wotereyu saganizirapo za masiku a moyo wake, chifukwa Mulungu amamutanganidwitsa ndi chisangalalo cha mu mtima mwake.

Onani mutuwo Koperani




Mlaliki 5:20
12 Mawu Ofanana  

pakuti udzaiwala chisoni chako, udzachikumbukira ngati madzi opita.


Zochepa zake za wolungama zikoma koposa kuchuluka kwao kwa oipa ambiri.


Ndipo muzitumikira Yehova Mulungu wanu, potero adzadalitsa chakudya chako, ndi madzi ako; ndipo ndidzachotsa nthenda pakati pa iwe.


Pali choipa ndachiona kunja kuno chifalikira mwa anthu,


Inu mukomana ndi iye amene akondwerera, nachita chilungamo, iwo amene akumbukira Inu m'njira zanu; taonani Inu munakwiya, ndipo ife tinachimwa; takhala momwemo nthawi yambiri, kodi tidzapulumutsidwa?


Popeza tsono tayesedwa olungama ndi chikhulupiriro, tikhala ndi mtendere ndi Mulungu mwa Ambuye wathu Yesu Khristu;


Popeza simunatumikire Yehova Mulungu wanu ndi chimwemwe ndi mokondwera mtima, chifukwa cha kuchuluka zinthu zonse;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa