Mlaliki 11:4 - Buku Lopatulika4 Woyang'ana mphepo sadzafesa; ndi wopenya mitambo sadzakolola. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Woyang'ana mphepo sadzafesa; ndi wopenya mitambo sadzakolola. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Amene ayembekeza kuti mphepo ikhale bwino, kapena kuti mitambo ibwere bwino, sadzabzala ndipo sadzakolola kanthu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Amene amayangʼana mphepo sadzadzala; amene amayangʼana mitambo sadzakolola. Onani mutuwo |