Mlaliki 11:3 - Buku Lopatulika3 Mitambo ikadzala mvula, itsanulira pansi; mtengo ukagwa kumwera pena kumpoto, pomwe unagwa mtengowo udzakhala pomwepo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Mitambo ikadzala mvula, itsanulira pansi; mtengo ukagwa kumwera pena kumpoto, pomwe unagwa mtengowo udzakhala pomwepo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Mitambo ikadzaza ndi madzi, kumagwa mvula. Mtengo ukagwera chakumwera kapena chakumpoto, kumene wagwerako kogonera nkomweko. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Ngati mitambo yadzaza ndi madzi, imagwetsa mvula pa dziko lapansi. Mtengo ukagwera cha kummwera kapena cha kumpoto, ndiye kuti udzagonera kumene wagwerako. Onani mutuwo |