Mlaliki 11:2 - Buku Lopatulika2 Gawira asanu ndi awiri ngakhale asanu ndi atatu; pakuti sudziwa choipa chanji chidzaoneka pansi pano. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Gawira asanu ndi awiri ngakhale asanu ndi atatu; pakuti sudziwa choipa chanji chidzaoneka pansi pano. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Ndalama zako uzisungize pa malo angapo, malo ambiri ndithu, pakuti sukudziŵa choipa chimene chidzaoneke pa dziko lapansi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Ndalama zako uzisungitse kwa anthu asanu ndi awiri, inde kwa anthu asanu ndi atatu, pakuti sudziwa ndi tsoka lanji limene likubwera pa dziko. Onani mutuwo |