Mlaliki 11:1 - Buku Lopatulika1 Ponya zakudya zako pamadzi; udzazipeza popita masiku ambiri. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Ponya zakudya zako pamadzi; udzazipeza popita masiku ambiri. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Ndalama zako uziike pa malonda okagulitsa kutsidya kwa nyanja, ndipo udzapeza phindu patapita masiku ambiri. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Ponya chakudya chako pa madzi, udzachipezanso patapita masiku ambiri. Onani mutuwo |