Mlaliki 1:11 - Buku Lopatulika11 Zoyamba zija sizikumbukiridwa; ngakhale zomwe zilinkudzazo, omwe adzakhalabe m'tsogolomo, sadzazikumbukirai. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Zoyamba zija sizikumbukiridwa; ngakhale zomwe zilinkudzazo, omwe adzakhalabe m'tsogolomo, sadzazikumbukirai. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Zakale sizikumbukika, ngakhale zinthu zimene zidzachitike pambuyo pake sizidzakumbukikanso ndi amene adzabwere m'tsogolo mwake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Anthu akale sakumbukiridwa, ngakhale amene adzabwera mʼtsogolomu sadzakumbukiridwa ndi iwo amene adzabwere pambuyo pawo. Onani mutuwo |