Mlaliki 1:10 - Buku Lopatulika10 Kodi pali kanthu unganene kuti, Taona katsopano aka? Kanalipo kale, kale lomwe tisanabadwe ife. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Kodi pali kanthu unganene kuti, Taona katsopano aka? Kanalipo kale, kale lomwe tisanabadwe ife. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Kodi chilipo chinthu chimene wina anganene kuti, “Ichi ndiye nchatsopano?” Iyai, chidaalipo kale, ifenso kukadalibe nkomwe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Kodi chilipo chinthu chimene wina anganene kuti, “Taona! Ichi ndiye chatsopano?” Chinalipo kale, kalekale; chinalipo ife kulibe. Onani mutuwo |