Mateyu 5:3 - Buku Lopatulika3 Odala ali osauka mumzimu; chifukwa uli wao Ufumu wa Kumwamba. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Odala ali osauka mumzimu; chifukwa uli wao Ufumu wa Kumwamba. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 “Ngodala anthu amene ali osauka mumtima mwao, pakuti Ufumu wakumwamba ndi wao. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 “Odala ndi amene ali osauka mu mzimu, chifukwa ufumu wakumwamba ndi wawo. Onani mutuwo |