Mateyu 5:4 - Buku Lopatulika4 Odala ali achisoni; chifukwa adzasangalatsidwa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Odala ali achisoni; chifukwa adzasangalatsidwa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Ngodala anthu amene akumva chisoni, pakuti Mulungu adzaŵasangalatsa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Odala ndi amene ali achisoni, chifukwa adzatonthozedwa. Onani mutuwo |