Mateyu 5:5 - Buku Lopatulika5 Odala ali akufatsa; chifukwa adzalandira dziko lapansi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Odala ali akufatsa; chifukwa adzalandira dziko lapansi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Ngodala anthu ofatsa, pakuti Mulungu adzaŵapatsa dziko la pansi pano kuti likhale lao. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Odala ndi amene ali ofatsa, chifukwa adzalandira dziko lapansi. Onani mutuwo |