Masalimo 98:1 - Buku Lopatulika1 Muimbireni Yehova nyimbo yatsopano; popeza anachita zodabwitsa: Dzanja lake lamanja, mkono wake woyera, zinamchitira chipulumutso. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Muimbireni Yehova nyimbo yatsopano; popeza anachita zodabwitsa: Dzanja lake lamanja, mkono wake woyera, zinamchitira chipulumutso. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Imbirani Chauta nyimbo yatsopano, popeza kuti wachita zodabwitsa. Dzanja lake lamanja ndi mkono wake woyera zampambanitsa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Imbirani Yehova nyimbo yatsopano, pakuti Iyeyo wachita zinthu zodabwitsa; dzanja lake lamanja ndi mkono wake woyera zamuchitira chipulumutso. Onani mutuwo |