Masalimo 97:12 - Buku Lopatulika12 Kondwerani mwa Yehova, olungama inu; ndipo yamikani pokumbukira chiyero chake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Kondwerani mwa Yehova, olungama inu; ndipo yamikani pokumbukira chiyero chake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Inu ndi anthu a Chauta, kondwerani mwa iye, ndipo mumthokoze potchula dzina lake loyera. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Kondwerani mwa Yehova Inu olungama ndipo tamandani dzina lake loyera. Onani mutuwo |