Masalimo 98:2 - Buku Lopatulika2 Yehova anawadziwitsira chipulumutso chake; anaonetsera chilungamo chake pamaso pa amitundu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Yehova anawadziwitsira chipulumutso chake; anaonetsera chilungamo chake pamaso pa amitundu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Chauta waonetsa kuti Iye wapambana pa nkhondo, waulula pamaso pa anthu a mitundu yonse kuti Iye ndi wolungama. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Yehova waonetsa chipulumutso chake ndipo waulula chilungamo chake kwa anthu a mitundu ina. Onani mutuwo |