Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 97:8 - Buku Lopatulika

8 Ziyoni anamva nakondwera, nasekerera ana aakazi a Yuda; chifukwa cha maweruzo anu, Yehova.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

8 Ziyoni anamva nakondwera, nasekerera ana akazi a Yuda; chifukwa cha maweruzo anu, Yehova.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

8 Anthu a ku Ziyoni akumva, ndipo akusangalala, midzi ya ku Yuda nayonso ikukondwera chifukwa cha kaweruzidwe kanu, Inu Chauta.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

8 Ziyoni akumva ndipo akukondwera, midzi ya Yuda ikusangalala chifukwa cha maweruzo anu Yehova.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 97:8
13 Mawu Ofanana  

Iye ndiye Yehova Mulungu wathu; maweruzo ake akhala padziko lonse lapansi.


Likondwere phiri la Ziyoni, asekere ana aakazi a Yuda, chifukwa cha maweruzo anu.


Zungulirani Ziyoni, ndipo muuzinge, werengani nsanja zake.


Ndipo olungama adzachiona, nadzaopa, nadzamseka, ndi kuti,


Wolungama adzakondwera pakuona kubwezera chilango, adzasamba mapazi ake m'mwazi wa woipa.


Pakuti Yehova watonthoza mtima wa Ziyoni, watonthoza mtima wa malo ake onse abwinja; ndipo wasandutsa chipululu chake ngati Edeni, ndi malo ake ouma ngati munda wa Yehova; kukondwa ndi kusangalala kudzapezedwa m'menemo, mayamikiro, ndi mau a nyimbo yokoma.


Taonani, Yehova walalikira kufikira malekezero a dziko lapansi. Nenani kwa mwana wamkazi wa Ziyoni, Taona chipulumutso chako chifika; taona mphotho yake ali nayo, ndi ntchito yake ili pamaso pake.


Kondwera kwambiri, mwana wamkazi wa Ziyoni; fuula mwana wamkazi wa Yerusalemu; taona, Mfumu yako ikudza kwa iwe; ndiye wolungama, ndi mwini chipulumutso; wofatsa ndi wokwera pabulu, ndi mwana wamphongo wa bulu.


Kondwera pa iye, m'mwamba iwe, ndi oyera mtima, ndi atumwi, ndi aneneri inu; chifukwa Mulungu anauweruzira kuweruzidwa kwanu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa