Masalimo 97:7 - Buku Lopatulika7 Onse akutumikira fano losema, akudzitamandira nao mafano, achite manyazi: Mgwadireni Iye, milungu yonse inu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Onse akutumikira fano losema, akudzitamandira nao mafano, achite manyazi: Mgwadireni Iye, milungu yonse inu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Onse opembedza milungu yonama, amene amanyadira mafano achabechabe, amachititsidwa manyazi, pakuti milungu ina yonse imagonjera Chauta. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Onse amene amalambira mafano osema amachititsidwa manyazi, iwo amene amanyadira mafano; mulambireni, inu milungu yonse! Onani mutuwo |