Masalimo 97:6 - Buku Lopatulika6 Kumwamba kulalikira chilungamo chake, ndipo mitundu yonse ya anthu ipenya ulemerero wake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Kumwamba kulalikira chilungamo chake, ndipo mitundu yonse ya anthu ipenya ulemerero wake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Zakumwamba zimalalika za kulungama kwake, ndipo anthu a mitundu yonse amaona ulemerero wake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Mayiko akumwamba amalengeza za chilungamo chake, ndipo mitundu yonse ya anthu imaona ulemerero wake. Onani mutuwo |