Masalimo 97:10 - Buku Lopatulika10 Inu okonda Yehova, danani nacho choipa: Iye asunga moyo wa okondedwa ake; awalanditsa m'manja mwa oipa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Inu okonda Yehova, danani nacho choipa: Iye asunga moyo wa okondedwa ake; awalanditsa m'manja mwa oipa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Chauta amakonda anthu odana ndi zoipa. Iye amasunga moyo wa anthu ake oyera mtima. Amaŵapulumutsa kwa anthu oipa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Iwo amene amakonda Yehova adane ndi zoyipa pakuti Iye amayangʼanira miyoyo ya amene amamukhulupirira ndipo amawapulumutsa mʼdzanja la anthu oyipa Onani mutuwo |