Masalimo 97:11 - Buku Lopatulika11 Kuunika kufesekera wolungama, ndi chikondwerero oongoka mtima. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Kuunika kufesekera wolungama, ndi chikondwerero oongoka mtima. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Amaŵalira anthu amene amamumvera, ndipo anthuwo amakhaladi ndi chimwemwe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Kuwala kumafika pa anthu olungama, ndi chimwemwe kwa olungama mtima. Onani mutuwo |