Masalimo 96:6 - Buku Lopatulika6 Pamaso pake pali ulemu ndi ukulu. M'malo opatulika mwake muli mphamvu ndi zochititsa kaso. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Pamaso pake pali ulemu ndi ukulu. M'malo opatulika mwake muli mphamvu ndi zochititsa kaso. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Ulemu ndi ufumu zili pamaso pake. Mphamvu ndi kukongola zili m'Nyumba mwake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Ulemu ndi ufumu zili pamaso pake, mphamvu ndi ulemerero zili mʼmalo ake opatulika. Onani mutuwo |