Masalimo 96:5 - Buku Lopatulika5 Pakuti milungu yonse ya mitundu ya anthu ndiyo mafano, koma Yehova analenga zakumwamba. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Pakuti milungu yonse ya mitundu ya anthu ndiyo mafano, koma Yehova analenga zakumwamba. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Paja milungu yonse ya mitundu ina ya anthu ndi mafano chabe. Koma Chauta ndiye adalenga zakumwamba. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Pakuti milungu yonse ya anthu a mitundu ina ndi mafano, koma Yehova analenga mayiko akumwamba. Onani mutuwo |