Masalimo 96:7 - Buku Lopatulika7 Mpatseni Yehova, inu, mafuko a mitundu ya anthu, mpatseni Yehova ulemerero ndi mphamvu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Mpatseni Yehova, inu, mafuko a mitundu ya anthu, mpatseni Yehova ulemerero ndi mphamvu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Tamandani, inu anthu a mitundu yonse, vomerezani kuti ulemerero ndi mphamvu, zonse nzake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Perekani kwa Yehova, inu mabanja a anthu a mitundu ina, perekani kwa Yehova ulemerero ndi mphamvu. Onani mutuwo |