Masalimo 96:2 - Buku Lopatulika2 Muimbireni Yehova, lemekezani dzina lake; lalikirani chipulumutso chake tsiku ndi tsiku. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Muimbireni Yehova, lemekezani dzina lake; lalikirani chipulumutso chake tsiku ndi tsiku. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Imbirani Chauta, tamandani dzina lake! Lalikani za chipulumutso chake tsiku ndi tsiku. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Imbirani Yehova, tamandani dzina lake; lalikirani chipulumutso chake tsiku ndi tsiku. Onani mutuwo |