Masalimo 96:3 - Buku Lopatulika3 Fotokozerani ulemerero wake mwa amitundu; zodabwitsa zake mwa mitundu yonse ya anthu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Fotokozerani ulemerero wake mwa amitundu; zodabwitsa zake mwa mitundu yonse ya anthu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Lengezani za ulemerero wake kwa anthu a mitundu yonse, simbani za ntchito zake zodabwitsa kwa anthu a m'maiko onse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Lengezani ulemerero wake pakati pa mayiko, ntchito zake zodabwitsa pakati pa mitundu yonse ya anthu. Onani mutuwo |