Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 93:3 - Buku Lopatulika

3 Mitsinje ikweza, Yehova, mitsinje ikweza mkokomo wao; mitsinje ikweza mafunde ao.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

3 Mitsinje ikweza, Yehova, mitsinje ikweza mkokomo wao; mitsinje ikweza mafunde ao.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

3 Inu Chauta, nyanja zazikulu zakwera, zikukokoma koopsa. Mafunde ake akuchita mkokomo waukulu.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

3 Nyanja zakweza Inu Yehova, nyanja zakweza mawu ake; nyanja zakweza mafunde ake ochita mkokomo.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 93:3
17 Mawu Ofanana  

Zingwe za imfa zinandizinga, ndipo mitsinje ya zopanda pake inandiopsa.


Chinkana madzi ake akokoma, nachita thovu, nagwedezeka mapiri ndi kudzala kwake.


Pali mtsinje, ngalande zake zidzakondweretsa mzinda wa Mulungu. Malo oyera okhalamo Wam'mwambamwamba.


Kumwamba kukondwere nilisekerere dziko lapansi; nyanja ibume mwa kudzala kwake.


Pakuti inu mudzatuluka ndi kukondwa, ndi kutsogozedwa ndi mtendere; mapiri ndi zitunda, zidzaimba zolimba pamaso panu, ndi mitengo yonse ya m'thengo idzaomba m'manja mwao.


Pakuti munandiponya mwakuya m'kati mwa nyanja, ndipo madzi anandizinga; mafunde anu onse a nyondonyondo anandimiza.


Ndipo njokayo inalavula m'kamwa mwake, madzi ngati mtsinje, potsata mkazi, kuti mkaziyo akakokoleredwe nao.


Ndipo anena ndi ine, Madziwo udawaona uko akhalako mkazi wachigololoyo ndiwo anthu, ndi makamu, ndi mitundu, ndi manenedwe.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa