Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 93:4 - Buku Lopatulika

4 Yehova Wam'mwamba ndiye wamphamvu, wakuposa mkokomo wa madzi ambiri, ndi mafunde olimba a nyanja.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

4 Yehova Wam'mwamba ndiye wamphamvu, wakuposa mkokomo wa madzi ambiri, ndi mafunde olimba a nyanja.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

4 Chauta amene ali pamwamba, ndi wamphamvu kupambana kulindima kwa madzi ambiri, ndi wamphamvu kuposa mafunde am'nyanja.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

4 Yehova ndi wamphamvu kupambana mkokomo wa madzi ambiri, ndi wamphamvu kupambana mafunde a nyanja, Yehova mmwamba ndi wamphamvu.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 93:4
9 Mawu Ofanana  

ndi kuti, Ufike mpaka apa, osapitirirapo; apa adzaletseka mafunde ako odzikuza?


Liu la Yehova ndi lamphamvu; liu la Yehova ndi lalikulukulu.


Amene atontholetsa kukuntha kwa nyanja, kukuntha kwa mafunde ake, ndi phokoso la mitundu ya anthu.


Pakuti kuli yani kuthambo timlinganize ndi Yehova? Afanana ndi Yehova ndani mwa ana a amphamvu?


Inu ndinu wakuchita ufumu pa kudzikuza kwa nyanja; pakuuka mafunde ake muwachititsa bata.


Koma Inu, Yehova, muli m'mwamba kunthawi yonse.


Kodi simundiopa Ine? Ati Yehova: simudzanthunthumira pamaso pa Ine, amene ndinaika mchenga chilekaniro cha nyanja, ndi lemba lamuyaya kuti isapitirirepo? Ndipo ngakhale mafunde ake achita gavigavi, alephera; ngakhale akokoma, sangathe kupitirirapo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa