Masalimo 93:2 - Buku Lopatulika2 Mpando wachifumu wanu ukhazikika kuyambira kale lija; Inu ndinu wosayambira ndi kale lomwe. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Mpando wachifumu wanu ukhazikika kuyambira kale lija; Inu ndinu wosayambira ndi kale lomwe. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Mpando wanu waufumu, Inu Chauta, mudaukhazikitsa kuyambira makedzana, Inu ndinu amuyaya. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Mpando wanu waufumu unakhazikika kalekale; Inu ndinu wamuyaya. Onani mutuwo |