Masalimo 92:7 - Buku Lopatulika7 chakuti pophuka oipa ngati msipu, ndi popindula ochita zopanda pake; chitero kuti adzaonongeke kosatha. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 chakuti pophuka oipa ngati msipu, ndi popindula ochita zopanda pake; chitero kuti adzaonongeke kosatha. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 ngakhale anthu oipa aziphuka ngati udzu, ndipo anthu ochimwa zinthu ziziŵayendera bwino, kwao nkuwonongeka kwamuyaya. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 kuti ngakhale anthu oyipa aphuka ngati udzu ndipo anthu onse ochita zoyipa apindula, adzawonongedwa kwamuyaya. Onani mutuwo |