Masalimo 87:3 - Buku Lopatulika3 Mzinda wa Mulungu, inu, akunenerani zakukulemekezani. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Mudzi wa Mulungu, inu, akunenerani zakukulemekezani. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Iwe mzinda wa Mulungu, anthu amakamba zambiri zotamanda iwe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Za ulemerero wako zimakambidwa, Iwe mzinda wa Mulungu: Sela Onani mutuwo |