Masalimo 87:4 - Buku Lopatulika4 Ndidzatchula Rahabu ndi Babiloni kwa iwo ondidziwa Ine; taonani, Filistiya ndi Tiro pamodzi ndi Kusi; uyu anabadwa komweko. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Ndidzatchula Rahabu ndi Babiloni kwa iwo ondidziwa Ine; taonani, Filistiya ndi Tiro pamodzi ndi Kusi; uyu anabadwa komweko. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Amati, “Pakati pa amene amandidziŵa, ndikutchula Rahabu ndi Babiloni. Ponena za dziko la Filistiya, Tiro ndi Etiopiya, anthu amati, ‘Uje adabadwira kumeneko.’ ” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 “Ndidzanena za Rahabe ndi Babuloni pakati pa iwo amene amandidziwa. Dzikonso la Filisitiya, Turo pamodzi ndi Kusi, ndipo ndidzati, ‘Uyu anabadwira mʼZiyoni.’ ” Onani mutuwo |
taonani, Ine, ndidzatuma ndi kutenga mabanja onse a kumpoto, ati Yehova, ndipo ndidzatuma kwa Nebukadinezara mfumu ya ku Babiloni, mtumiki wanga, ndipo ndidzatengera iwo padziko lino, ndi pa okhalamo ake onse, ndi pa mitundu iyi yozungulira, ndipo ndidzathetsa iwo ndithu, ndi kuwayesa iwo chizizwitso, ndi chotsonyetsa, ndi bwinja lamuyaya.